收聽Mumford & Sons的Ngamila歌詞歌曲

Ngamila

Mumford & Sons, Baaba Maal, The Very Best2016年6月17日

Ngamila 歌詞

Ngamila - Mumford & Sons/Baaba Maal/The Very Best

Lyrics by:Mumford/Sons/The Very Best

Composed by:Mumford/Sons/The Very Best

Produced by:Mumford/Sons/Johan Hugo

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Umafuna nthawi zonse uvutike moyo wonse

Kufuna zonse zabwino zikhale zako

Ufunefune bwanji sungalikwanitse dzikoli

Mapeto ake ndikunenetsa udzagonje ndiwe

You search all your life

Stealing all you find

And you stare at your own hands

Not the hands they entwine

Pokuti upeze chuma mpakana kukhwima

Kunzunitsa mzi kuwataya ku moto

Kufunsafunsa mudzi Ngamila yanga ili kuti

Chonsecho wakwera ngati wachitila dala

Allo saiero hore uye you want meet go

Med bekli ma

Tine anno saiero what you mind annu nuwa

Der benne ma

Sarilo wasa vaiur nitu der benne ma

Eto horrepaa eur niddo der benne ma

Pokuti upeze chuma mpakana kukhwima

Kunzunitsa mzi kuwataya ku moto

Kufunsafunsa mudzi Ngamila yanga ili kuti

Chonsecho wakwera ngati wachitila dala

You have all you need

When you're held by me

Don't pine for what's not

And whatever will be

You have all you need

When you're held by me

Don't pine for what's not

And whatever will be

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

Ngamila yanga ili kuti

 

Ngamila yanga ili kuti